Unduna wa za ulimi wakhazikitsa ntchito yopereka feteleza wangongole kwa alimi a m’ma boma a Chikwawa ndi Nsanje. Ntchitoyi ili pansi pa bungwe la National...
Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, wati boma likuyesetsa kuti anthu onse amene akhudzidwa ndi njala akhale ndi chakudya posatengera dera limene...
Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Micheal Usi, afika m’dziko muno mawa atakhala nawo pa mwambo olumbilitsa mtsogoleri wa tsopano wa dziko la Mozambique,...
Ophunzira akale apa sukulu ya Mzuzu University apereka K2.9 million kwa ophunzira osowa apa sukuluyi ndicholinga chakuti iwathandizire fizi komanso zinthu zina. Amene wayimira mkulu...
Aphungu anyumba ya malamulo m’chigawo chapakati ayamika ntchito yogawa fetereza wangongole amene bungwe la Economic Empowerment Fund (NEEF) likupereka kwa alimi. Mwa zina, aphunguwa amene...
Bungwe la Agriculture Commercialisation (AGCOM) lathandiza kutukula gulu la alimi limene akulitcha kuti ‘Team North Cooperative’ lochokera ku Lupaso munzinda wa Mzuzu. Poyankhula pamene nduna...
Kefasi Chitsala waku Cobbe Barracks ku Zomba ndi yemwe wakhala katswiri wampikisano wa chaka chino wa asilikali a m’dziko muno wothamanga mtunda wa ma kilomita...