Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Nkhani

OYIMBA OMWE ANALI PANSI PA NDE’FEYO AIMBA LERO KU BLANTYRE

Zokonzekera zonse za phwando la mayimbidwe limene likutchedwa kuti Nde’feyo legacy, lomwe lichitikire ku 24/7 ku Blantyre lero, zili mchimake.

Mwambowu ubweretsa pamodzi oyimba asanu amene anasayinidwa ndi kampani ya Nde’feyo pomwe ankayamba kuyimba monga Maskal, Piksy, Onesimus, Trumel ndi Bucci.

Poyankhula ndi MBC, mmodzi wa oyimba-wa, Maskal, yemwe wabwera m’dziko muno kuchokera ku America komwe amakhala, wati anthu akonzekere mayimbidwe apamwamba.

Wolemba: Simeon Boyce

Related posts

Namondwe Chido wakula mphamvu

Romeo Umali

Dr Usi ayamikira mpingo wa Anglican pothandizira boma pa chitukuko

Romeo Umali

Dziko la Malawi latsegula ofesi ya ukazembe ku Israel

Blessings Kanache
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.