Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Tifikireni nthawi zonse -OPC

Ofesi yoona zofalitsa nkhani mu ofesi ya mlembi wamkulu wa boma ndi nduna OPC yalangiza atolankhani kuti apitirize kugwira  bwino ntchito ndi boma.

Mneneri wa ofesi yi, a Robert Kalindidza ndiomwe anena izi ku Mulanje pamsonkhano waukulu wapa chaka wa atolankhani achikatolika m’dziko muno.

A Kalindidza ati atolankhani amagwira ntchito yayikulu yofalitsa mauthenga  ndi ndikuzindikiritsa anthu kotero ndi bwenzi leni leni la boma pa chitukuko.

Poyankhulapo, wachiwiri kwa wamkulu wa bungweli mayi Josephine Chinele ati bungwe la Association of Catholic Journalists-ACJ lachita zinthu zochuluka pothandidza  pa chitukuko chadziko lino monga kuthandidza  anthu ovutika  munthawi ya ngozi  zogwa  mwadzidzi

Related posts

MERP to reform basic education

Romeo Umali

China supports KCH with medical equipment

Romeo Umali

President Chakwera ayamikira ntchito yokonza msewu wa M1

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.