Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Sports Sports

Mwaungulu tsopano adzivala Jersey 11

Osewera kutsogolo wa timu ya FCB Nyasa Big Bullets, Patrick Mwaungulu, amupatsa nambala 11 yomwe adzivala pa Malaya ake a timuyi.

Izi zadziwika mu chikalata chimene atulutsa a timu ya Bullets pamene amatulutsa m’ndandanda wa osewera a timuyi mu chaka cha 2024.

Mwaungulu amusintha kuchoka pa nambala 29 yomwe amupatsa Chawanangwa Gumbo, amene poyamba amavala nambala 31.

Osewera ena monga Clyde Senaji, Richard Chimbamba, Yankho Singo, Kenneth Pasuwa ndi Ephraim Kondowe nawonso awasinthira nambala zawo.

Related posts

Malawi thump Seychelles to reach Beach Soccer semi-finals

Rabson Kondowe

Seven busted for possession of cannabis in Mzimba

MBC Online

CRWB ipereka mphoto kwa makasitomala okhulupirika

Yamikani Simtowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.