Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Mtukula pakhomo ndi popumira — Sendeza

Nduna yoona kuti pasamakhale kusiyana pantchito pakati pa amuna ndi akazi, a Jean Sendeza, ati kukhazikitsidwa kwa mtukula pakhomo wa m’mizinda ndi chitsimikizo choti mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wadzipereka kuonetsetsa kuti anthu apeze popumira pamene boma likukonza chuma cha dziko lino.

Mai Sendeza anena izi ku Zomba kumene ntchito yokhazikitsa mtukula pakhomo wa m’mizinda ya K15.7 billion ili mkati.

Iwo apempha anthu omwe akusankha opindula kuti asamakondere palembana maina.

Related posts

MW, ZIM EXPLORE NEW AREAS OF COOPERATION

Mayeso Chikhadzula

Malawi secures K140 billion to foster development

Rabson Kondowe

ATI INVESTS K5BN IN LUANAR CROP RESEARCH

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.