Malawi Broadcasting Corporation
News Nkhani

Mtukula pakhomo wammizinda ukhazikitsidwa lero

Boma likukhazikitsa mtukula pakhomo wammizinda lero.

Ntchito yokhazikitsa ntchito ya mtukula pakhomo wa mmizinda,imene ndiya ndalama zokwana K15.7 billion, ili mkati mu mzinda wa Zomba.

Kudzera mu ndondomekoyi, mabanja okwana 105,000 alandira ndalama zokwana K150,000 pakamodzi kuti alimbane ndi umphawi.

Nduna ya zachuma, a Simplex Chithyola Banda, nduna yoona kuti pasamakhale kusiyana pakati pa amayi ndi abambo, a Jean Sendeza, komanso mlembi wa zachuma Professor Betchani Tchereni, ali nawo pa mwambowu.

Related posts

Tobacco sales at K677 billion

Romeo Umali

President Chakwera in Mzuzu, calls for unity of purpose

MBC Online

Women urged to collaborate for financial independence

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.