Mrongozgi wa charo chino, Dr Lazarus Chakwera, wakhazikiska committee ya nduna kuti yendeske nyifwa ya wachiwiri kwa mrongozgi wa charo chino, chipondi Dr Saulos Chilima.
Mtsogoleri wa bungwe loyang’anira masewero a mpira wa miyendo padziko lonse la pansi la FIFA, a Gianni Infantino, akuyembekezeka kupepesa mwapadera ku banja la malemu
President Dr Lazarus Chakwera has constituted a ministerial committee to oversee the state funeral of Vice President and eight others who were killed in a
Mtsogoleri wa zipani zotsutsa kunyumba ya malamulo, a George Chaponda, wati ali ndi chisoni chifukwa cha imfa ya wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Malemu
Apolisi limodzi ndi azachipatala ayamba kunyamula matupi a anthu amene ataya miyoyo yawo pangozi ya ndege imene yagwa chapa Lunjika mu nkhalango ya Chikangawa m’boma
Anthu osiyanasiyana ayamba kufika kunyumba ya wachiwiri kwa mtsogoleri wadziko lino, Malemu Dr Saulos Chilima, ku Area 12 munzinda wa Lilongwe. Ena mwa anthuwa ndi
Mrongozgi wa charo chino Dr Lazarus Chakwera wati wachiwiri kwa mrongozgi wa charo chino, Dr Saulos Chilima, lumoza na wanyawo wankhondi na wanayi- 9 wafwa