Category : Nkhani
Bullets dhoovirikana, okhwaokhwave
Mulhoko wamphirameto wa FCB Nyasa Big Bullets wookelhemulhiwa ni Silver Strikers vamatheelha ayo yeereyelha va Kamuzu Stadium o Blantyre. Chinsisi Maonga amulhoko wa Silver Strikers...
Dr Chilima afika m’dziko la Korea
Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Saulos Chilima tsopano wafika m’dziko la Republic of Korea kumene akachite nawo msonkhano waukulu pakati pa dzikolo ndi...
Masamba ndi Tcheta afwafwanthana madzulo ano
Kuvumba mabindula madzulo ano pa Kamuzu Institute of Sports pakati pa ziphona zazigogodo ziwiri Limbani Masamba komanso Simeon Tcheta pa nkhonya yolimbirana lamba yomwe yakonzedwa...
NEEF yati ipitilira kuthandiza anthu
Bungwe la National Economic Empowerment Fund (NEEF) latsimikiza kuti lipitiriza ntchito yothandiza anthu, kuphatikizapo amene anakhudzidwa ndi kusefukira kwa madzi m’dziko muno. Wapampando wa bungweli,...
Manoma eriwa elhopwelhopwe yaakumana ni evithevithe
Inenelhi dha Mighty Mukuru Wanderers dhohaatuthilha omulhihani athokothoko amulhoko wa Premier Bet Dedza Dynamos vamatheelha ayo yeereya va Kamuzu Stadium o Blantyre. Chistopher Kumwembe sika...
Dr Chakwera ati akufuna kubwezeretsa zomwe zinaonongeka
Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wati chidwi chake chili pobwezeretsa zinthu zomwe anthu akhala akuononga m’buyomu kuti chuma chadziko lino chibwelere m’chimake, momwe...
Chipani cha ANC chikutsogola ku South Africa
Bungwe loyendetsa chisankho mdziko la South Africa mawa lamulungu lilengeza zotsatira zonse zotsimikizika zachisankho pomwe latsala pang’ono kumalizitsa ntchito yowerengera mavoti. Pakadali pano, chipani cholamula...
Tiwapatsa mwayi wa ngongole kuti apeze mpamba — TEVETA
Pofuna kuwonetsetsa kuti achinyamata amene amaliza maphunziro a ulimi wa zipatso, masamba, maluwa ndi mbewu zina pa sukulu ya Corporate Institute of Horticulture (CIH) ali...

