Category : Nkhani
Timakhulupilira mtendere – MCP
Chipani cha Malawi Congress (MCP) chati sichikhala nawo ku msonkhano waukulu wa chipani cha United Democratic Front (UDF) potsatira mphekesera yoti zipani zina zotsutsa zachita...
‘Ntchito ya maphunziro ndi umoyo wabwino m’sukulu ikonzedwenso’
Bungwe la Save the Children lati ntchito za maphunziro ndi umoyo wabwino m’sukulu za m’dziko muno zikufunika kuunikidwa ndikukonzedwanso mwakuya komanso mwamakono pofuna kuthana ndi...
Tilimbikitse chikhalidwe ndikusunga mbiri ya Malawi – MAGLA.
Bungwe lomwe limayang’anira ntchito za masewera a mulosera la Malawi Gaming and Lotteries Authority (MAGLA) lati ntchito yolimbikitsa miyambo ya chikhalidwe ikuyenera kuthandiziridwa mokwanira pofuna...
USAID yatsanzika mwapamwamba ku Fisheries
Mawu oti pochoka pamsasa saipitsa ndi amene yagwira bungwe la USAID imene yapereka galimoto zitatu zandalama pafupifupi K380 million ndi katundu wina ku nthambi yoona...
Chitukuko chisaononge chilengedwe
Nduna yoona zamalo, a Deus Gumba, apempha anthu omwe amagwira ntchito yoyeza malo mdziko muno kuti atenge udindo oteteza zachilengedwe akamagwira ntchito zawo. Ndunayi yanena...
Mafumu ayamikira ndondomeko yolembetsa malo
Mafumu a m’boma la Blantyre ayamikira boma pokhazikitsa ntchito yolembetsa umwini wa malo. Mfumu yayikulu Kunthembwe inati ntchito yolembetsa maloyi ndi yabwino kwambiri kaamba kakuti...

