Category : Nkhani
Ayamikira Dr Chakwera posankha mabodi atsopano a kampani zaboma
Ena mwa atsogoleri amipingo m’dziko muno ati mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera waonetsa kusakondera kwake posankha anthu atsopano m’ma board a kampani za...
Ndife okondwa kuti boma limatiika mmapulani ake – Ras Mwanamanga
Wachiwiri kwa nduna yaza ulimi Benedicto Chambo anacheza ndi akuluakulu achipembezo chachi Rasta munzinda wa Lilongwe. A Chambo, omwenso ndi phungu wadera la Mangochi –...
Chimwendo Banda ayamika Chakwera poyika amayi m’maudindo akuluakulu
Mtsogoleri wa zokambirana mu nyumba ya malamulo, a Richard Chimwendo Banda, wayamika mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera chifukwa chokhala ndi chikhulupiliro mwa amayi...
Akatswiri amalamulo ati ulendo wa Kabambe ukadalipo
Akatswiri pa nkhani zamalamulo a Justin Dzonzi ndi a Allan Ntata ati ntchito ikadalipo kwa amene akutsogolera chipani cha UTM, a Dalitso Kabambe, pa nkhani...
Greenbelt yapereka ntchito yomanga Nthola-Ilola
Bungwe la Greenbelt Initiative Authority lapereka ntchito ya gawo lachiwiri lomanga malo a mthilira a Nthola-Ilola m’boma la Karonga kwa amene agwire ntchitoyi, a Kabiki...
Eni galimoto akondwa ndi dongosolo lokonza msewu wa Makanjira
Bungwe la Transporters Association of Malawi lati kukonza msewu wa Mangochi-Makanjira kudzathandizanso kwambiri kulimbikitsa ntchito za mtengatenga ndi malonda pakati pa dziko lino ndi la...
Anthu aku Nsalu ku Lilongwe awalangiza kuti akavotere Dr Lazarus Chakwera pa chisankho cha chaka chino kuti zitukuko zipitilire.
Mlembi wamkulu wa chipani cha Malawi Congress (MCP), yemwenso ndi nduna ya maboma ang’ono, umodzi ndi chikhalidwe, a Richard Chimwendo Banda, ndiye wanena izi ndikulimbikitsa...