Author : Timothy Kateta
413 Posts -
0 Comments
Malawi to preserve wildlife
Malawi has vowed to play its part in the protection and conservation of wildlife within the Southern African Development Community (SADC) region. Minister of Tourism,...
Akatswiri amalamulo ati ulendo wa Kabambe ukadalipo
Akatswiri pa nkhani zamalamulo a Justin Dzonzi ndi a Allan Ntata ati ntchito ikadalipo kwa amene akutsogolera chipani cha UTM, a Dalitso Kabambe, pa nkhani...
Eni galimoto akondwa ndi dongosolo lokonza msewu wa Makanjira
Bungwe la Transporters Association of Malawi lati kukonza msewu wa Mangochi-Makanjira kudzathandizanso kwambiri kulimbikitsa ntchito za mtengatenga ndi malonda pakati pa dziko lino ndi la...
Chakwera commended on Presidential interactions
Former moderator of the CCAP Livingstonia Synod, Reverend Mezuwa Banda, has commended President Dr Lazarus Chakwera for his continued interest in engaging various stakeholders and...
Greenbelt Authority yakhutira ndi kuchuluka kwa chimanga
Bungwe la Greenbelt Authority lati ndi lokhutitsidwa ndi kuchulukwa kwa chimanga chomwe bungweli lalima ku imodzi mwa ma Mega Farm ya Chikwawa Irrigation Scheme m’boma...
Aloza chala maboma akale posalabadira nsewu wa Karonga-Chiweta
Anthu ena adzudzula maboma a m’mbuyomu kaamba kosalabadira nsewu wa Karonga-Chiweta umene boma lapereka K5 billion ku kampani ya SOS Construction kuti awukonzenso. Pothirapo ndemanga...
NEEF iyamba kugawa ngongole za ulimi wamthilira
Bungwe la NEEF lati liri mkati mokonza ndondomeko zoti likhale likugawa ngongole ya zaulimi wa mthirira kuyambira mwezi wa April chaka chino. Mkulu wa bungweli,...
Ulimi wamakono udzathetsa njala — Kawale
Nduna yoona za ulimi a Sam Kawale yauza alangizi kuti adzitenga gawo lalikulu losintha kaganizidwe ka anthu ndi cholinga chothana ndi vuto lakusowa kwa chakudya...

