Akatswiri pa nkhani zamalamulo a Justin Dzonzi ndi a Allan Ntata ati ntchito ikadalipo kwa amene akutsogolera chipani cha UTM, a Dalitso Kabambe, pa nkhani...
Bungwe la Transporters Association of Malawi lati kukonza msewu wa Mangochi-Makanjira kudzathandizanso kwambiri kulimbikitsa ntchito za mtengatenga ndi malonda pakati pa dziko lino ndi la...
Former moderator of the CCAP Livingstonia Synod, Reverend Mezuwa Banda, has commended President Dr Lazarus Chakwera for his continued interest in engaging various stakeholders and...
Bungwe la Greenbelt Authority lati ndi lokhutitsidwa ndi kuchulukwa kwa chimanga chomwe bungweli lalima ku imodzi mwa ma Mega Farm ya Chikwawa Irrigation Scheme m’boma...
Anthu ena adzudzula maboma a m’mbuyomu kaamba kosalabadira nsewu wa Karonga-Chiweta umene boma lapereka K5 billion ku kampani ya SOS Construction kuti awukonzenso. Pothirapo ndemanga...
Bungwe la NEEF lati liri mkati mokonza ndondomeko zoti likhale likugawa ngongole ya zaulimi wa mthirira kuyambira mwezi wa April chaka chino. Mkulu wa bungweli,...
Nduna yoona za ulimi a Sam Kawale yauza alangizi kuti adzitenga gawo lalikulu losintha kaganizidwe ka anthu ndi cholinga chothana ndi vuto lakusowa kwa chakudya...
Black Economic Empowerment Movement is urging the government to increase funds to the National Economic Employment Fund (NEEF) to reach out to more farmers with...