Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Walipira chindapusa chifukwa chonyoza wodwala AIDS

Khoti lina ku Balaka lalamula bambo wazaka 45, Frank Nazombe, kuti apereke chindapusa cha ndalama zokwana K65,000 chifukwa chonyoza mayi wodwala matenda a AIDS.

Mneneri wapolisi ku Balaka, a Gladson M’bumpha, wati Nazombe anayambana ndi mayiyo ku mowa.

Tsiku lotsatira, Nazombe analawira mammawa kupita kunyumba kwa mayiyo ndikuyamba kumunena kuti akudwala matenda a AIDS ndipo wafalitsa matendawo kwa amuna ochuluka mderalo.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

MACRA ALLOCATES NEW FM FREQUENCIES

MBC Online

Wapha mwana wa zaka zitatu chifukwa chodutsa mmunda mwake

MBC Online

Avokado urges musicians to collaborate for growth

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.