Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Walipira chindapusa chifukwa chonyoza wodwala AIDS

Khoti lina ku Balaka lalamula bambo wazaka 45, Frank Nazombe, kuti apereke chindapusa cha ndalama zokwana K65,000 chifukwa chonyoza mayi wodwala matenda a AIDS.

Mneneri wapolisi ku Balaka, a Gladson M’bumpha, wati Nazombe anayambana ndi mayiyo ku mowa.

Tsiku lotsatira, Nazombe analawira mammawa kupita kunyumba kwa mayiyo ndikuyamba kumunena kuti akudwala matenda a AIDS ndipo wafalitsa matendawo kwa amuna ochuluka mderalo.

 

Related posts

Mamaland unveils K346BN project in Nkhata-Bay

Romeo Umali

Chakwera to officially open International Blantyre Cancer Centre

Secret Segula

Climate smart beneficiaries asked to invest in village savings loans in Likoma

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.