Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Nyakwawa ikakhala ku ndende pamlandu wogwililira

Khoti la Magistrate ku Phalombe lalamula nyakwawa Nayuma, yomwe dzina lake ndi Leonard Julius, kukakhala kundende zaka 12 chifukwa chogwililira mtsikana wazaka 14.

Mneneri wapolisi ku Phalombe, Jimmy Kapanja, wati izi zinadziwika mwezi wa October chaka chatha.

Malinga ndi a Kapanja, pakadali pano mtsikanayo, yemwe amadwala matenda a mu ubongo, ali ndi mwana wa nyakwawayo.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Chiwerengero cha omwalira kwa Manase chafika pa 7

Blessings Kanache

FAM launches 2023 National Women’s Football championship

Romeo Umali

Govt assures Malawians of improved livelihoods

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.