Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Nyakwawa ikakhala ku ndende pamlandu wogwililira

Khoti la Magistrate ku Phalombe lalamula nyakwawa Nayuma, yomwe dzina lake ndi Leonard Julius, kukakhala kundende zaka 12 chifukwa chogwililira mtsikana wazaka 14.

Mneneri wapolisi ku Phalombe, Jimmy Kapanja, wati izi zinadziwika mwezi wa October chaka chatha.

Malinga ndi a Kapanja, pakadali pano mtsikanayo, yemwe amadwala matenda a mu ubongo, ali ndi mwana wa nyakwawayo.

 

Related posts

Beach Soccer Malawi saddened by Kaluwa’s demise

Romeo Umali

Finance Minister commissions 10 boreholes in Balaka

Romeo Umali

Malawi lauded for empowering smallholder farmers

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.