Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Nyakwawa ikakhala ku ndende pamlandu wogwililira

Khoti la Magistrate ku Phalombe lalamula nyakwawa Nayuma, yomwe dzina lake ndi Leonard Julius, kukakhala kundende zaka 12 chifukwa chogwililira mtsikana wazaka 14.

Mneneri wapolisi ku Phalombe, Jimmy Kapanja, wati izi zinadziwika mwezi wa October chaka chatha.

Malinga ndi a Kapanja, pakadali pano mtsikanayo, yemwe amadwala matenda a mu ubongo, ali ndi mwana wa nyakwawayo.

 

Related posts

PCL urges private sector to boost production

Rabson Kondowe

‘Tili okondwa ndi zitukuko za Dr Chakwera’

Rabson Kondowe

Chitipa United falls short at home against Creck SC

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.