Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Nyakwawa ikakhala ku ndende pamlandu wogwililira

Khoti la Magistrate ku Phalombe lalamula nyakwawa Nayuma, yomwe dzina lake ndi Leonard Julius, kukakhala kundende zaka 12 chifukwa chogwililira mtsikana wazaka 14.

Mneneri wapolisi ku Phalombe, Jimmy Kapanja, wati izi zinadziwika mwezi wa October chaka chatha.

Malinga ndi a Kapanja, pakadali pano mtsikanayo, yemwe amadwala matenda a mu ubongo, ali ndi mwana wa nyakwawayo.

 

Related posts

Mutharika pushes for deeper Malawi–China cooperation

MBC Online

Chithyola calls on legislators to provide oversight role on budget

McDonald Chiwayula

MLS reintroduces law journal after 12 years

Secret Segula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.