Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

‘Thetsani nkhanza kwa anthu achialubino’

Bungwe la Standing Voice lapempha aMalawi kuti achilimike pothandiza kuthetsa nkhanza zomwe anthu ena amachitira anthu achialubino pomaimba lamya ku ma nambala awulele, kupereka uthenga akaona nkhanzazi.

Ma nambalawo ndi 4293, 116, 5600 ndi 6600.

Atsogoleri a bungweli, limene limalimbikitsa ufulu wa anthu a chialubino, anena izi pa misonkhano yomwe akhala akuchita limodzi ndi bungwe la YONECO m’boma la Mulanje ndi cholinga chophunzitsa anthu za ufulu wa anthuwa.

Mabungwewoo akugwira ntchitoyi limodzi ndi apolosi komanso nthambi ya boma yoona zachisamaliro cha anthu.

 

Related posts

Piksy gears up for new album

Romeo Umali

Chipatala cha South Lunzu chikupempha thandizo

Romeo Umali

Bushiri apereka chimanga kwa mabanja 200 ku Mangochi

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.