Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

‘Thetsani nkhanza kwa anthu achialubino’

Bungwe la Standing Voice lapempha aMalawi kuti achilimike pothandiza kuthetsa nkhanza zomwe anthu ena amachitira anthu achialubino pomaimba lamya ku ma nambala awulele, kupereka uthenga akaona nkhanzazi.

Ma nambalawo ndi 4293, 116, 5600 ndi 6600.

Atsogoleri a bungweli, limene limalimbikitsa ufulu wa anthu a chialubino, anena izi pa misonkhano yomwe akhala akuchita limodzi ndi bungwe la YONECO m’boma la Mulanje ndi cholinga chophunzitsa anthu za ufulu wa anthuwa.

Mabungwewoo akugwira ntchitoyi limodzi ndi apolosi komanso nthambi ya boma yoona zachisamaliro cha anthu.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Chitipa registers more cholera cases

MBC Online

Government recruits and promotes secondary school teachers

MBC Online

Helios Towers ready to help Malawi achieve SDG

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.