Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Anthu oposa 600 atuluka DPP ndikulowa MCP ku Mulanje

Anthu omwe anali mamembala a chipani cha DPP okwana 619 ochokera m’madera a kummwera komanso pakati m’boma la Mulanje, alengeza kuti atuluka chipanichi ndipo alowa Malawi Congress (MCP).

Mmodzi wa akuluakulu a MCP, a Brown Mpinganjira, Wapampando wa chipanichi ku Mulanje komanso wachiwiri kwa mkulu wa achinyamata mchipani cha MCP, a Blessings Chilembwe, ndiwo alandira anthuwa pamwambo umene unachitika pa Mulanje paboma.

Related posts

Tonse titengepo gawo, atero a Chakwera

Alinafe Mlamba

MUSCCO yachita phindu lokwana K82 billion

Romeo Umali

Bambo agwililira mwana

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.