Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Kambwiri ayikidwa mmanda mawa

Thupi la amene anali mkhalakale pa nkhani zoulutsa mawu, Joshua Kambwiri, alitengera ku mudzi kwawo ku Domasi m’boma la Zomba, kumene akaliyike m’manda mawa Lolemba.

Mwambo wa mapemphero otsanzikana ndi malemu Kambwiri unachitikira pa tchalitchi cha Ngumbe CCAP ku Chileka munzinda wa Blantyre kumene malemuwa amapemphera.

Malemu Kambwiri, amene anagwirapo ntchito ku nyumba youlutsa mawu ya MBC, amwalira ali ndi zaka 62.

Related posts

NGO drills 500 boreholes in the Southern Region

Romeo Umali

Equals Project to improve science subjects pass rate in CDSS

Mayeso Chikhadzula

AMBASSADOR YOUNG RETIRES

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.