Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Anthu oposa 600 atuluka DPP ndikulowa MCP ku Mulanje

Anthu omwe anali mamembala a chipani cha DPP okwana 619 ochokera m’madera a kummwera komanso pakati m’boma la Mulanje, alengeza kuti atuluka chipanichi ndipo alowa Malawi Congress (MCP).

Mmodzi wa akuluakulu a MCP, a Brown Mpinganjira, Wapampando wa chipanichi ku Mulanje komanso wachiwiri kwa mkulu wa achinyamata mchipani cha MCP, a Blessings Chilembwe, ndiwo alandira anthuwa pamwambo umene unachitika pa Mulanje paboma.

Related posts

Ophunzira pa UNIMA akhazikitsa kampani ya luso lamakono

Rabson Kondowe

MCP ikhazikisa mfundo za chitukuko

Romeo Umali

Mia athandiza mabanja 3000 ndi chakudya ku Chikwawa

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.