Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Zaka zitatu pogulitsa makala mosatsata lamulo

Khothi la Magistrate mu mzinda wa Blantyre la lamula kuti abambo atatu akagwire ukayidi kwa zaka ziwiri komanso chaka ndi theka kaamba kopezeka olakwa pochita malonda ogulitsa makala opanda chiphaso komanso kuzembetsa zinthu za munkhalango.

Popereka chigamulo, Magistrate Godfrey Balaka anati zilango zonsezi ziyendera limodzi pofuna kuti anthu ena atengerepo phunziro ndipo mlanduwu adapalamula pa 17 April, 2024.

Nthambi za boma monga Police, ACB ndi nthambi ya zankhalango padakali pano zikugwira limodzi ntchito yothandiza kuteteza zachilengedwe.

#MBCDigital
#Manthu

Print Friendly, PDF & Email

Author

  • Mayeso Chikhadzula joined MBC in 2006, he's an Investigative Journalist and Principal Reporter. He's also a News Anchor, Presenter, and producer.

Related posts

Bangwe appoints Kajawa as Coach

Romeo Umali

Two nabbed over K145.2 million robbery

Romeo Umali

Environmental NGO calls for stronger reforestation drive

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.