Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

‘Tili okondwa ndi zitukuko za Dr Chakwera’

Mfumu yayikulu Nsabwe ya m’boma la Thyolo yathokoza mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera kaamba kogawa zitukuko m’madera onse mosayang’ana nkhope.

Mfumuyi yati mwazina, anthu a m’dera lake ndi okondwa ndi ndalama za mtukula pakhomo zomwe akulandira.

“Mudzitiyendera pafupipafupi ife mafumu ndi anthu adera lino tigwira ntchito ndi boma,” iwo anatero.

Iwo amayankhula pamene membala wamkulu wa chipani cha Malawi Congress, a Brown Mpinganjira, akuchititsa msonkhano pa Mathiya ku Thekerani m’bomalo.

 

Olemba : Geoffrey Chinawa

Related posts

M1 Road rehabilitation near Kabula Police Station resumes

Romeo Umali

Dr. Chakwera Commissions Nyika-Vwaza Gravity fed Water Scheme

Romeo Umali

Dr Chakwera ayamikira anthu ku Nsanje posamukira kumtunda

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.