Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

‘Masomphenya a Chilima sangafe’

Wachiwiri kwa mtsogoleri wadziko lino, Dr Micheal Usi, alonjeza kuti apitiriza masomphenya achitukuko a malemu Dr Saulosi Chilima.

Iwo ati agwirizana kale ndi Prezidenti Dr Lazarus Chakwera kuti masomphenya achitukuko a malemu Chilima asafe.

Iwo amayankhula izi kwa khamu limene lawayimitsa pa Kameza ku Blantyre kuti awayankhule.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

Chakwera urges hard work over handouts

Rabson Kondowe

LWB targets better water services with new strategic plan

McDonald Chiwayula

Self-upgraded teachers to compete in promotional interviews —Govt

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.