Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Prezidenti Chakwera ayendera chitukuko m’boma la Mzimba

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero apita m’boma la Mzimba kumene ayendere ntchito yomanga bwalo lazamasewero la M’mbelwa kudzanso ofesi za khonsolo ya M’mbelwa m’bomalo.

Dr Chakwera akafikanso kulikulu la Inkosi yamakhosi M’mbelwa.

Mtsogoleri wa dziko linoyu akucheza m’chigawo chakumpoto ndikuyendera ntchito za chitukuko zosiyanasiyana.

Related posts

Anthu apitilira kukhuza maliro a bambo Kapusa

Blessings Kanache

Gawo lachitatu la kalembera wazisankho wayamba

Romeo Umali

Adzudzula aphungu kamba kosapereka ulemu kwa Sipikala

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.