Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Prezidenti Chakwera ayendera chitukuko m’boma la Mzimba

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero apita m’boma la Mzimba kumene ayendere ntchito yomanga bwalo lazamasewero la M’mbelwa kudzanso ofesi za khonsolo ya M’mbelwa m’bomalo.

Dr Chakwera akafikanso kulikulu la Inkosi yamakhosi M’mbelwa.

Mtsogoleri wa dziko linoyu akucheza m’chigawo chakumpoto ndikuyendera ntchito za chitukuko zosiyanasiyana.

Related posts

CTS Courier yati ikufuna kupereka mwayi watchito kwa achinyamata

Rabson Kondowe

Mwambo wa chikumbutso wayamba ku Mulanje

Romeo Umali

Sitima ina yonyamula mafuta iyamba kuyenda sabata ya mawa

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.