Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Prezidenti Chakwera ayendera chitukuko m’boma la Mzimba

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero apita m’boma la Mzimba kumene ayendere ntchito yomanga bwalo lazamasewero la M’mbelwa kudzanso ofesi za khonsolo ya M’mbelwa m’bomalo.

Dr Chakwera akafikanso kulikulu la Inkosi yamakhosi M’mbelwa.

Mtsogoleri wa dziko linoyu akucheza m’chigawo chakumpoto ndikuyendera ntchito za chitukuko zosiyanasiyana.

Related posts

Alexander ‘Cage’ Likande wamwalira

Romeo Umali

GEFT ichepetsa mavuto obwera ndi kusintha kwa nyengo — Boma, UNDP

Romeo Umali

Dr Chilima afika m’dziko la Korea

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.