Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Prezidenti Chakwera akhala nawo pa mwambo operekeza maliro

Anthu ochuluka asonkhana ku nyumba ya chisoni ya Sunset Funeral Services ku Kanengo munzinda wa Lilongwe komwe pali chikonzero chonyamula ena mwa matupi a anthu omwe adafa pangozi ya ndege limodzi ndi wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, malemu Dr Saulos Chilima.

Pali chiyembekezo choti pa mwambowu pakhalanso mwambo wa Misa poremekeza mzimu wa mayi Patricia Shanil Dzimbiri, omwe anaakhalapo mayi wa dziko lino zaka za mmbuyomu.

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, komanso mayi wa dziko lino, Madam Monica Chakwera, akuyembekezeka kukhala nawo pamwambowu.

 

Print Friendly, PDF & Email

Author

  • Mayeso Chikhadzula joined MBC in 2006, he's an Investigative Journalist and Principal Reporter. He's also a News Anchor, Presenter, and producer.

Related posts

Girl killed in Nkhata Bay road accident

MBC Online

KATSONGA  COURTS UNCDF ON INVESTMENT OPPORTUNITIES

McDonald Chiwayula

Daka, Katchomoza at the helm of MRA

Justin Mkweu
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.