Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Prezidenti Chakwera akhala nawo pa mwambo operekeza maliro

Anthu ochuluka asonkhana ku nyumba ya chisoni ya Sunset Funeral Services ku Kanengo munzinda wa Lilongwe komwe pali chikonzero chonyamula ena mwa matupi a anthu omwe adafa pangozi ya ndege limodzi ndi wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, malemu Dr Saulos Chilima.

Pali chiyembekezo choti pa mwambowu pakhalanso mwambo wa Misa poremekeza mzimu wa mayi Patricia Shanil Dzimbiri, omwe anaakhalapo mayi wa dziko lino zaka za mmbuyomu.

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, komanso mayi wa dziko lino, Madam Monica Chakwera, akuyembekezeka kukhala nawo pamwambowu.

 

Related posts

Between thirst and death in Chilomoni as Cholera sets in

Rabson Kondowe

Justice Ministry for a strong legal framework on Assets Declaration

Rabson Kondowe

Aloza chala maboma akale posalabadira nsewu wa Karonga-Chiweta

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.