Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Ntchito yodinda ma pasipoti yayambiranso ku Mzuzu

Nthambi yoona zolowa ndi kutukuka mdziko muno ya Immigration yalengeza zakuyambanso kwa ntchito yodinda ndikupereka ziphaso zoyendera mchigawo chakumpoto.

Malinga ndi chikalata chomwe wasayinira ndi mneneri kunthambiyi a Wellington Chiponde, kuyambira lolemba pa 29 July anthu ofuna mapasipoti tsopano atha kufika ku Mzuzu dongosolo lonse loyenerera kuti akhale ndi chiphasochi.

Nthambi ya Immigration yakhala isakudinda ziphaso zoyendera kwanthawi ndipo yayamikira anthu kaamba kakudekha kwawo panthawiyi.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

MZUNI alumni yapereka K2.9M kwa ophunzira osowa

MBC Online

VILLAGE HEADMAN SLAPPED 20-YEAR SENTENCE FOR RAPE

MBC Online

Summit of the future consultative meeting underway

Austin Fukula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.