Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Ntchito yodinda ma pasipoti yayambiranso ku Mzuzu

Nthambi yoona zolowa ndi kutukuka mdziko muno ya Immigration yalengeza zakuyambanso kwa ntchito yodinda ndikupereka ziphaso zoyendera mchigawo chakumpoto.

Malinga ndi chikalata chomwe wasayinira ndi mneneri kunthambiyi a Wellington Chiponde, kuyambira lolemba pa 29 July anthu ofuna mapasipoti tsopano atha kufika ku Mzuzu dongosolo lonse loyenerera kuti akhale ndi chiphasochi.

Nthambi ya Immigration yakhala isakudinda ziphaso zoyendera kwanthawi ndipo yayamikira anthu kaamba kakudekha kwawo panthawiyi.

Related posts

Petroleum importers provides safe water to Linyangwa Health Centre

Romeo Umali

Konzekerani ulimi wa fodya — Tobacco Commission

Romeo Umali

Pre-budget consultations commence today

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.