Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Ntchito yodinda ma pasipoti yayambiranso ku Mzuzu

Nthambi yoona zolowa ndi kutukuka mdziko muno ya Immigration yalengeza zakuyambanso kwa ntchito yodinda ndikupereka ziphaso zoyendera mchigawo chakumpoto.

Malinga ndi chikalata chomwe wasayinira ndi mneneri kunthambiyi a Wellington Chiponde, kuyambira lolemba pa 29 July anthu ofuna mapasipoti tsopano atha kufika ku Mzuzu dongosolo lonse loyenerera kuti akhale ndi chiphasochi.

Nthambi ya Immigration yakhala isakudinda ziphaso zoyendera kwanthawi ndipo yayamikira anthu kaamba kakudekha kwawo panthawiyi.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Sign language can develop Malawi — SLID

Juliana Mlungama

Police arrest Mwanamvekha, four others in Salima Sugar syndicate

Eunice Ndhlovu

UNFPA GIVES NSO K60M WORTH ICT GADGETS

Trust Ofesi
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.