Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Manja SDA ikutsekera msonkhano wa Misasa

Mpingo wa Manja Seventh Day Adventist mu nzinda wa Blantyre lero ukumalizitsa msonkhano wake wa pachaka wa Misasa omwe unayamba pa 27 August 2024.

Mutu wa msonkhanowu ndi ‘Kusandulika mu chikhalidwe pomwe tikukatumikira’.

Mlaliki wa mkulu pa msonkhanowu ndi mtsogoleri wakale wa Seventh Day Adventist m’dziko muno, abusa Frackson Kuyama.

Mu ulaliki wawo iwo anayamba ndi kulangiza akhristu kuti adzikhala ololerana posasungirana mangawa, kukhala okhutira ndi zomwe ali nazo komanso kusamalira chakudya.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Quech Nursing Officer urges support for patients

Chisomo Break

BEACH SOCCER ASSOCIATION FEELS NEGLECTED

MBC Online

FIRST LADY HAILS MUSLIM WORLD LEAGUE FOR PUMPING K8.5 BN FOR ORPHANS’ EDUCATION SUPPORT

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.