Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Mwambo wachionetsero cha zokopa alendo wayamba

Mwambo wa chionetsero cha ntchito zokopa alendo komanso chikhalidwe wayamba ndi ulendo wa ndawala kuchokera pa Memorial Tower mpakana mu msewu wa Presidential Drive munzinda wa Lilongwe.

Mwambowu, umene wakonzedwa ndi bungwe la Malawi Tourism Council, cholinga chake ndi kulimbikitsa ntchito zokopa alendo ndi chikhalidwe m’dziko muno.

Mfumu ya mnzinda wa Lilongwe, a Esther Sagawa, komanso akuluakulu ena ochita malonda okopa alendo ndi oyimba osiyanasiyana monga Lulu ali nawo pa mwambowu.

 

Related posts

Musamvere andale abodza, ogawa mitundu — Chimwendo Banda

Romeo Umali

New solar initiative to boost MSMEs and drive economic growth

McDonald Chiwayula

Burning Spear atsanzikana ndi anthu asanapume kuimba

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.