Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Mwambo wachionetsero cha zokopa alendo wayamba

Mwambo wa chionetsero cha ntchito zokopa alendo komanso chikhalidwe wayamba ndi ulendo wa ndawala kuchokera pa Memorial Tower mpakana mu msewu wa Presidential Drive munzinda wa Lilongwe.

Mwambowu, umene wakonzedwa ndi bungwe la Malawi Tourism Council, cholinga chake ndi kulimbikitsa ntchito zokopa alendo ndi chikhalidwe m’dziko muno.

Mfumu ya mnzinda wa Lilongwe, a Esther Sagawa, komanso akuluakulu ena ochita malonda okopa alendo ndi oyimba osiyanasiyana monga Lulu ali nawo pa mwambowu.

 

Related posts

Okweza dala mitengo ya katundu nthawi yawo yatha — Mumba

MBC Online

WHO introduces Hepatitis C Self-Test Kit

Romeo Umali

IPOR empowers Zomba CBOs

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.