Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Mwambo wachionetsero cha zokopa alendo wayamba

Mwambo wa chionetsero cha ntchito zokopa alendo komanso chikhalidwe wayamba ndi ulendo wa ndawala kuchokera pa Memorial Tower mpakana mu msewu wa Presidential Drive munzinda wa Lilongwe.

Mwambowu, umene wakonzedwa ndi bungwe la Malawi Tourism Council, cholinga chake ndi kulimbikitsa ntchito zokopa alendo ndi chikhalidwe m’dziko muno.

Mfumu ya mnzinda wa Lilongwe, a Esther Sagawa, komanso akuluakulu ena ochita malonda okopa alendo ndi oyimba osiyanasiyana monga Lulu ali nawo pa mwambowu.

 

Related posts

Inkosi M’mbelwa yadzudzula ndale zonyozana

MBC Online

Tea sector’s future hinges on supporting smallholder farmers – FAO

McDonald Chiwayula

Kayira tells Mabedi to adopt attacking football

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.