The United Nations Children’s Fund (UNICEF), through its partner Gavi, has donated three brand new Toyota land cruiser vehicles and 3,000 bicycles worth K1.2 billion...
Prezidenti wadziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wati ndikofunika kuti makontalakitala adzigwira ntchito zapamwamba ndi zolimba. Pa chifukwachi, Dr Chakwera walamula mlembi mu ofesi ya Prezidenti...
The Senior Magistrate Court in Mangochi has ordered Mary Julius Saidi,24 and Molly Kainga,34 to pay fines after they were convicted on six counts each...
Nthambi yoona za nyengo m’dziko muno yatsimikiza kuti namondwe Filipo safika m’dziko muno. Nthambiyi yati namondweyu akuyenda mobwelera ku nyanja ya mchere ya India, komwe...
Mphunzitsi wakale wa timu ya FOMO, Mapopa ‘Kent’ Msukwa, walangiza timuyi kuti isapusitsike ikasewera bwino ndi m’khala kale za timu ya pfuko lino ya Flames,...
Vice Chancellor for the Lilongwe University of Agriculture and Natural Resources (LUANAR), Professor Emmanuel Kaunda, has emphasized the need for Malawi to invest in innovation...
Lilongwe Police Station has detained two individuals on suspicion that they orchestrated a fraudulent scheme, resulting in the loss of K750,000 by a local businessman....
Bungwe la Malawi Revenue Authority (MRA) lati likwanitsa kutolera ndalama zokwana K2.18 trillion mu chaka cha boma cha 2023/2024 chimene chikutha kumapeto a mwezi uno....
The Federation of Disability Organisations in Malawi (FEDOMA) has called for a more inclusive approach in the management of natural disasters in the country. Speaking...
The Tobacco Association of Malawi (TAMA) is optimistic about favourable pricing in this year’s tobacco marketing season. According to a statement from the industry regulator...