Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News Nkhani

Msonkho pa ma belo wabwerera kuzakale

Mkulu wabungwe lotolera misonkho, a John Biziwick, walamula kuti ogwira ntchito kubungweli aleke kugwiritsa ntchito msonkho okwera pa mabelo a zovala, umene anaukhazikitsa posachedwapa.

Izi zikudza patangodutsa nthawi yochepa ochita malonda amtunduwu munzinda wa Lilongwe atachita zionetsero ndikukapereka madandaulo awo ku ofesi za bungweli.

Related posts

Rumphi conducts measles immunization exercise

Rabson Kondowe

Malawi launches First Foods Africa Initiative to combat child food poverty

McDonald Chiwayula

MERA CAUTIONS ON ILLEGAL FUEL VENDING AND HOARDING

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.