Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News Nkhani

Msonkho pa ma belo wabwerera kuzakale

Mkulu wabungwe lotolera misonkho, a John Biziwick, walamula kuti ogwira ntchito kubungweli aleke kugwiritsa ntchito msonkho okwera pa mabelo a zovala, umene anaukhazikitsa posachedwapa.

Izi zikudza patangodutsa nthawi yochepa ochita malonda amtunduwu munzinda wa Lilongwe atachita zionetsero ndikukapereka madandaulo awo ku ofesi za bungweli.

Related posts

YOUTHFUL LEGISLATORS URGED TO EMULATE JZU

MBC Online

DSTV SERVICES RESUMES FRIDAY- MACRA

Blessings Kanache

Ngabu Vehicle Inspection Station to open this month

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.