Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Ochita malonda achita zionetsero ku Lilongwe

Ochita malonda a zovala zakaunjika mu mnzinda wa Lilongwe akuchita zionetsero kamba kakukwera kwa misonkho pa mabelo a zovalazi.

Pakali pano, ochita malondawa afika pa ofesi ya bungwe lotolera misonkho ya Malawi Revenue Authority (MRA) komwe akudzatula zikalata zawo zamadandaulo.

 

Related posts

Malawi strides in early childhood nutrition

MBC Online

UNDUNA WAZA CHUMA UKULINGALILA ZOONJEZELA NDALAMA KUBUNGWE LA NEEF

MBC Online

President wa Guinea-Bissau akudzapepesa maliro a Dr Chilima ndi ena

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.