Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Ochita malonda achita zionetsero ku Lilongwe

Ochita malonda a zovala zakaunjika mu mnzinda wa Lilongwe akuchita zionetsero kamba kakukwera kwa misonkho pa mabelo a zovalazi.

Pakali pano, ochita malondawa afika pa ofesi ya bungwe lotolera misonkho ya Malawi Revenue Authority (MRA) komwe akudzatula zikalata zawo zamadandaulo.

 

Related posts

Akakhala kundende zaka 14 chifukwa chogwilira wamisala

Romeo Umali

SOS EMPOWERS 49 WOMEN WITH BUSINESS START UP SUPPORT

MBC Online

Tambala Super Cup ayikhazikitsa

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.