Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

CHITUKUKO CHIFIKIRE MADERA ONSE — ZIKHALE

Mmodzi wa akulu akulu mchipani cha MCP yemwenso ndi nduna yaza Chitetezo Chadziko a Ken Zikhale Ng’oma ati boma lipitiriza kutukula madera onse a dziko lino mosakondera potukula miyoyo ya anthu.

Mwachitsanzo,iwo anakamba za ntchito ya minda ikulu ikulu ya Mega Farms imene ikugwiridwa ku Machinga.

A Zikhale Ng’oma amayankhula pa bwalo laza masewero la Chaka ku Machinga pa msonkhano omwe anachititsa.

Mu kanema ali m’musiyu, akuonetsa zina zomwe a Ng’oma analankhula.

#MBCOnlineServices

Related posts

SCTP boosts livelihoods in Nkhata Bay

Romeo Umali

THE DREAD OF THE GOLDEN YEARS

McDonald Chiwayula

Malawi revives banana industry under FAO-China initiative

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.