Malawi Broadcasting Corporation
Culture Local News Nkhani Politics

‘Enock Chihana apepese’

Bungwe la Chewa Heritage Malawi – Chifukwato cha a Chewa lauza a Enock Chihana kuti apepese mtundu wa a Chewa pazimene adayankhula pamsonkhano wa olembankhani Lachitatu munzinda wa Lilongwe.

Iwo ati a Chihana adayankhula mawu achipongwe pa msonkhanowo.

Wapampando wa bungweli, Mfumu Sosola, ati bungwe lawo lapereka masiku atatu kwa a Chihana kuti apepese kupanda kutero adzawaitana kuti akawaonetse kudambwe.

Related posts

Ex-MBC, MANA intern constructs child care centres

Romeo Umali

CHAKWERA ATTENDS OFFICIAL LAUNCH OF THEOLOGY ASSOCIATION OF MALAWI

Mayeso Chikhadzula

Minister Hara calls for innovation within construction industry

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.