Malawi Broadcasting Corporation
Culture Local News Nkhani Politics

‘Enock Chihana apepese’

Bungwe la Chewa Heritage Malawi – Chifukwato cha a Chewa lauza a Enock Chihana kuti apepese mtundu wa a Chewa pazimene adayankhula pamsonkhano wa olembankhani Lachitatu munzinda wa Lilongwe.

Iwo ati a Chihana adayankhula mawu achipongwe pa msonkhanowo.

Wapampando wa bungweli, Mfumu Sosola, ati bungwe lawo lapereka masiku atatu kwa a Chihana kuti apepese kupanda kutero adzawaitana kuti akawaonetse kudambwe.

Related posts

MHEN urges border districts to screen entrants for mpox

Romeo Umali

Longest-serving remandee sentenced to 36 years imprisonment

MBC Online

Man jailed 18 years for robbery

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.