Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local News Nkhani Tourism

Sitima yapakati pa LL, BT iyambanso kuyenda — Hara

Nduna yaza mtengatenga, a Jacob Hara, yati sitima yoyenda pakati pa mizinda ya Blantyre ndi Lilongwe iyambiranso posachedwapa.

A Hara anati gawo lachiwiri ikhala kukonzanso njanji yolowera m’boma la Mchinji pofuna kulumikizitsana ndi dziko la Zambia.

Iwo ati izi zili chomwechi chifukwa akonza mlatho omwe unaduka zomwe zichititse kuti sitima iyambenso kuyenda.

Olemba : Patrick Dambula

Related posts

Self-upgraded teachers to compete in promotional interviews —Govt

Rabson Kondowe

MWASIP disburses K285 million to Zomba communities

Romeo Umali

Blue Eagles targets K13 million at fundraising dinner

Yamikani Simtowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.