Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local News Nkhani Tourism

Sitima yapakati pa LL, BT iyambanso kuyenda — Hara

Nduna yaza mtengatenga, a Jacob Hara, yati sitima yoyenda pakati pa mizinda ya Blantyre ndi Lilongwe iyambiranso posachedwapa.

A Hara anati gawo lachiwiri ikhala kukonzanso njanji yolowera m’boma la Mchinji pofuna kulumikizitsana ndi dziko la Zambia.

Iwo ati izi zili chomwechi chifukwa akonza mlatho omwe unaduka zomwe zichititse kuti sitima iyambenso kuyenda.

Olemba : Patrick Dambula

Related posts

Alimi musatengeke ndi mavenda – MUSCCO

Alinafe Mlamba

Thupi la Dr Chilima aliyika m’manda

Mayeso Chikhadzula

Kamtukule hopes to sell Malawi as perfect destination at US-Africa Summit

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.