Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local News Nkhani Tourism

Sitima yapakati pa LL, BT iyambanso kuyenda — Hara

Nduna yaza mtengatenga, a Jacob Hara, yati sitima yoyenda pakati pa mizinda ya Blantyre ndi Lilongwe iyambiranso posachedwapa.

A Hara anati gawo lachiwiri ikhala kukonzanso njanji yolowera m’boma la Mchinji pofuna kulumikizitsana ndi dziko la Zambia.

Iwo ati izi zili chomwechi chifukwa akonza mlatho omwe unaduka zomwe zichititse kuti sitima iyambenso kuyenda.

Olemba : Patrick Dambula

Related posts

Malawians urged to practice healthy lifestyles to combat oesophageal cancer

Rabson Kondowe

DoDMA rolls out disaster response clusters

Rabson Kondowe

Chakwera reaffirms commitment to development

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.