Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News Nkhani

Msonkho pa ma belo wabwerera kuzakale

Mkulu wabungwe lotolera misonkho, a John Biziwick, walamula kuti ogwira ntchito kubungweli aleke kugwiritsa ntchito msonkho okwera pa mabelo a zovala, umene anaukhazikitsa posachedwapa.

Izi zikudza patangodutsa nthawi yochepa ochita malonda amtunduwu munzinda wa Lilongwe atachita zionetsero ndikukapereka madandaulo awo ku ofesi za bungweli.

Related posts

CMC calls for clear, strategic gospel communication

McDonald Chiwayula

Zotsatira za mayeso a sitandade 8 ndi fomu 2 zatuluka

Alinafe Mlamba

MBC’S ENTERTAINERS OF THE YEAR TOP NOMINEES RELEASED

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.