Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Tipitiriza kuthandiza – NBS Bank

Bank ya NBS yathandiza anthu okalamba komanso a ulumali ndi matumba a ufa wa chimanga kummwera kwa boma la Chiradzulu.

Poyankhula popereka thandizoli, mkulu wa Branch ya Limbe, a Twaibu Nnani, ati bankiyi ipitiriza kuthandiza osowa kudzera mu njira zosiyanasiyana.

Ndipo mfumu yaikulu Mpunga yapempha mabungwe akufuna kwabwino kuti athandize mabanja omwe akhudzidwa ndi njala.

Malinga ndi a Mpunga thandizoli ati ndi lapafupifupi K3.5 million.

Wolemba: Blessings Cheleuka

 

Related posts

‘Andale asamalowelere ntchito zam’ma khonsolo’

Alinafe Mlamba

Tsimikizirani anthu kuti maziko onse achitukuko apindulira aliyense- Dr. Chakwera

Romeo Umali

Tonse titengepo gawo, atero a Chakwera

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.