Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Tonse titengepo gawo, atero a Chakwera

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wapempha aMalawi kuti atengepo gawo pa ntchito yokonzanso chuma cha dziko lino mu njira zosiyanasiyana monga kulimbika pa ntchito za ulimi.

Dr Chakwera watinso anthu ochita malonda akuyenera akhale ndi mwayi ofanana potenga ngongole kuchokera ku bungwe la NEEF kuti ntchito zamtunduwu zipindulire anthu onse.

Mtsogoleri wa dziko linoyu wayankhula izi kwa anthu omwe anaima pa Katoto Roundabout ku Mzuzu.

Wolemba: Musase Cheyo

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Mia adzudzula mchitidwe owononga zitukuko za madzi

Emmanuel Chikonso

Ana opyola 1,000 asiyira sukulu panjira ku Lilongwe m’miyezi ya April mpaka June

Lonjezo Msodoka

Mlandu authetsa, mavenda akufuna chipepeso

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.