Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Tonse titengepo gawo, atero a Chakwera

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wapempha aMalawi kuti atengepo gawo pa ntchito yokonzanso chuma cha dziko lino mu njira zosiyanasiyana monga kulimbika pa ntchito za ulimi.

Dr Chakwera watinso anthu ochita malonda akuyenera akhale ndi mwayi ofanana potenga ngongole kuchokera ku bungwe la NEEF kuti ntchito zamtunduwu zipindulire anthu onse.

Mtsogoleri wa dziko linoyu wayankhula izi kwa anthu omwe anaima pa Katoto Roundabout ku Mzuzu.

Wolemba: Musase Cheyo

Related posts

Madam Chakwera apempha mafumu kuti alimbikitse ana pa maphunziro

Rabson Kondowe

Khonsolo ya mnzinda wa Lilongwe ikuchotsa zinyanyala usiku uno

Alinafe Mlamba

Mia adzudzula mchitidwe owononga zitukuko za madzi

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.