Bungwe lotolera misonkho la Malawi Revenue Authority MRA lati likukumana ndi mavuto pa ntchito yotolera misonkho, maka pa galimoto zimene zimalowa m’dziko muno mozemba. Mkulu...
Msonkhano waukulu wa chipani cha People’s (PP) wayamba munzinda wa Lilongwe, komwe nthumwi za chipanichi zoposa 1000 zisankhe adindo atsopano. Wapampando wa komiti yomwe yakonza...
People in Dowa District under Senior Chief Msakambewa have hailed Mudzi Connect for helping the district with several developmental projects, including the construction of an...
Nthumwi 1,100 zochekera mzigawo zonse za dziko lino za chipani cha People’s zikuyembekeza kusankha atsogoleri atsopano a chipanichi pa msonkhano waukulu wa chipanichi, umene uyambe...
Boma la Japan lithandiza dziko la Malawi ndi mpunga wa matani okwana pafupifupi 1900, amene ndi matumba oposa 30,000, kuti agawire anthu amene alibe chakudya...
Key stakeholders are reviewing the Last Mile Infrastructure Pre-Feasibility Report for the Southern Africa Trade and Connectivity Project (SATCP) in Dowa. The meeting, chaired by...
Timu ya masewero a Draughts ya dziko lino yalephera kupita kukasewera nawo mpikisano wa dziko lonse kaamba kochedwa kukonzekera. Mlembi wa bungwe loyendetsa masewero wa...
Over 400 runners are set to take part in this year’s Blantyre 42.195 kilometre race on Saturday, a significant increase from last year’s 97 participants....