Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Timu ya Draughts yalephera kupita ku Russia

Timu ya masewero a Draughts ya dziko lino yalephera kupita kukasewera nawo mpikisano wa dziko lonse kaamba kochedwa kukonzekera.

Mlembi wa bungwe loyendetsa masewero wa m’dziko muno la ADIMA, Suzgo Nkhoma, wauza MBC kuti anachedwa kuchititsa mpikisano opeza akatswiri opita ku Russia kaamba kosowa ndalama ndipo izi zachititsa kuti alephere kupangitsa ma VISA a osewerawa mu nthawi  yabwino.

Osewera okwana asanu ndi amene amayenera kupita ku mpikisanowo.

A Nkhoma ati padakali pano, chidwi chonse ayika pa mpikisano wa m’mayiko a mu Africa omwe uchitike mwezi wa November m’dziko la Zimbabwe.

 

Olemba Amin Mussa

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Bishop Mtumbuka launches football tourney for peace

MACRA to combat hacking, fraud through new campaign

Emmanuel Chikonso

Tembo represents Dr Chakwera at Lapukeni’s funeral

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.