Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Usi ali ku mapemphero

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi akuchita nawo mapemphero pa mpingo wa Zambezi Evangelical ku Mitsidi mu mzinda wa Blantyre.

Pampingopa palinso chikondwerero chokhazikitsa mlembi wamkulu pa mpingowu, m’busa Robert Yanduya.

Dr Usi analandiridwa ndi abusa komanso akuluakulu ampingowu.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Katanda to launch book on mental health

Romeo Umali

UWC qualifies to CAF

MBC Online

Mfumu yayikulu Mwirang’ombe yayamikira sukulu ya ntchito zaluso lamanja ku Karonga

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.