Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Chakwera akhala nawo pa mapemphero a misa

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera pamodzi ndi mayi wa fuko lino Madam Monica Chakwera akuyembekezeka kukhala nawo pa mapemphero a misa pa mpingo wa katolika wa St. Peters mu mzinda wa Mzuzu.

Mtsogoleri wa dziko linoyu akuyembekezeka kufika pa mpingowu cha m’ma 10 koloko m’mawa uno.

Olemba: Jackson Sichali.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Kwacha holds firm against US Dollar

MBC Online

Child education advocate calls for trained caretakers

MBC Online

Habitual thief sentenced to eight years in jail

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.