Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Chakwera akhala nawo pa mapemphero a misa

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera pamodzi ndi mayi wa fuko lino Madam Monica Chakwera akuyembekezeka kukhala nawo pa mapemphero a misa pa mpingo wa katolika wa St. Peters mu mzinda wa Mzuzu.

Mtsogoleri wa dziko linoyu akuyembekezeka kufika pa mpingowu cha m’ma 10 koloko m’mawa uno.

Olemba: Jackson Sichali.

 

Related posts

RBM concerned over low uptake of insurance services

Romeo Umali

UNICEF remains committed to improve child services in Malawi

Romeo Umali

Partnership is a win-win situation — MBC DG

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.