Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Sports Sports

Queens yafa ndi South Africa

Queens yagonja 65-35 ndi South Africa mu mpikisano wa m’mayiko a mu Africa umene ukuchitikira m’dziko la Namibia.

Malawi, yomwe inagonjetsa Zambia mu masewero ake oyamba, inatsalira m’zigawo zonse zinayi za masewerowo.

Apa ndiye kuti timuyi ili pa nambala yachiwiri mu Gulu A momwe mulinso ma timu a Kenya ndi Zambia.

Ma timu awiri omwe amalize pamwamba pa gululi apitilira mu ndime ya semifainolo.

Timuyi isewera masewero ake omaliza a m’magulu lachinayi lino pomwe ikumane ndi timu ya Kenya.

Olemba: Amin Mussa

Related posts

Khonsolo ya Zomba ndiyokondwa ndi zitukuko

Romeo Umali

Crime rate in Limbe decreases by 14%

Romeo Umali

LL Magistrate’s Court fines woman K800,000 for possessing Marijuana

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.