Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Religion

Parish ya Nzama yakwana zaka 125

Kuli chikondwelero ku Parish ya mpingo wa Katolika ya Nzama m’boma la Ntcheu pamene akukhazikitsa nyengo yokondwelera kuti papita zaka 125 chiyikhazikitsireni.

Malinga ndi Bambo Godno Chinkanda a pa Parishiyi, malowa, amene ali m’dera la T/A Mpando, ndi ofunikira kwambiri mu mbiri ya a Katolika komanso dziko la Malawi.

Iwo ati, mwazina, kumeneku ndi kumene kunayambira sukulu ya ukachenjede ya katolika m’chaka cha 1902.

Ma mishonale a chi katolika anafika ku Nzama m’chaka cha 1901 pa 25 July.

Iwo ati chikondwelerochi chidzafika pa chimake m’chaka cha 2026.

 

Related posts

MNT promotes sustainable tobacco farming

McDonald Chiwayula

Mabedi urged to adopt aggressive football against Sao Tome & Principe

Romeo Umali

Over 29,000 students’ loan applications filed at Loans Board

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.