Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Religion

Parish ya Nzama yakwana zaka 125

Kuli chikondwelero ku Parish ya mpingo wa Katolika ya Nzama m’boma la Ntcheu pamene akukhazikitsa nyengo yokondwelera kuti papita zaka 125 chiyikhazikitsireni.

Malinga ndi Bambo Godno Chinkanda a pa Parishiyi, malowa, amene ali m’dera la T/A Mpando, ndi ofunikira kwambiri mu mbiri ya a Katolika komanso dziko la Malawi.

Iwo ati, mwazina, kumeneku ndi kumene kunayambira sukulu ya ukachenjede ya katolika m’chaka cha 1902.

Ma mishonale a chi katolika anafika ku Nzama m’chaka cha 1901 pa 25 July.

Iwo ati chikondwelerochi chidzafika pa chimake m’chaka cha 2026.

 

Related posts

WORLEC, Oxfam engage electoral stakeholders in Nsanje

Rabson Kondowe

Chakwera to launch construction of cost-effective classroom blocks

Romeo Umali

Malawi deserves easy access to financial investments — RBM

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.