Malawi Broadcasting Corporation
Environment Local Local News Nkhani

MVULA YABWERANSO

Nthambi yowona za nyengo m’dziko muno yati mvula ikhala ikugwa mpakana sabata ya mawa, pamene yayamba kuvumba m’maboma ambiri kuyambira loweruka m’mawa.

Ena ati zimenezi zitha kupangitsa kuti mbewu zosiyanasiyana, zimene zinayamba kunyala chifukwa cha ng’amba, zitsitsimuke pamene mvula yagwa.

Kubwera kwa mvulaku kwaika chikhulupiliro mea ambiri kuti mwina alimi akhoza kukolora mokwanira, zimene zingathandize kupewa njala.

Related posts

Pakachere calls on faith leaders to join fight against GBV

Alinafe Mlamba

‘Tiganizireni poonjezera ndalama za mtukula pakhomo’

MBC Online

Moroccan Embassy in Malawi commemorates 46th Anniversary of Green March

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.