Malawi Broadcasting Corporation
Environment Local Local News Nkhani

MVULA YABWERANSO

Nthambi yowona za nyengo m’dziko muno yati mvula ikhala ikugwa mpakana sabata ya mawa, pamene yayamba kuvumba m’maboma ambiri kuyambira loweruka m’mawa.

Ena ati zimenezi zitha kupangitsa kuti mbewu zosiyanasiyana, zimene zinayamba kunyala chifukwa cha ng’amba, zitsitsimuke pamene mvula yagwa.

Kubwera kwa mvulaku kwaika chikhulupiliro mea ambiri kuti mwina alimi akhoza kukolora mokwanira, zimene zingathandize kupewa njala.

Related posts

Musadalire kusewera ndi m’khala kale — Mapopa

Romeo Umali

Kaluwa to be laid to rest today

Alinafe Mlamba

Malawi applauded for advancing women’s role in climate innovation

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.