Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

M’modzi wamwaliranso ndi ‘ambuye tengeni’, apolisi amanga atatu

Chiwerengero cha anthu omwe amwalira atamwa mowa odziwika kuti ‘ambuye tengeni’ kwa Manase ku Blantyre tsopano chafika pa asanu ndi atatu 8.

Apolisi atsimikiza kuti amanga anthu atatu kamba kankhaniyi.

MBC itatsatira nkhaniyi lero yapezanso kuti anthu ena awiri ali mwakayakaya pa chipatala chachikulu cha Queen Elizabeth pomwe munthu mmodzi amutulutsa atachira.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Malemu Lapukeni awayika lero

MBC Online

Chakwera akhala nawo pa mapemphero a misa

MBC Online

OCP, USAID partners to improve Africa’s agricultural production

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.