Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

M’modzi wamwaliranso ndi ‘ambuye tengeni’, apolisi amanga atatu

Chiwerengero cha anthu omwe amwalira atamwa mowa odziwika kuti ‘ambuye tengeni’ kwa Manase ku Blantyre tsopano chafika pa asanu ndi atatu 8.

Apolisi atsimikiza kuti amanga anthu atatu kamba kankhaniyi.

MBC itatsatira nkhaniyi lero yapezanso kuti anthu ena awiri ali mwakayakaya pa chipatala chachikulu cha Queen Elizabeth pomwe munthu mmodzi amutulutsa atachira.

Related posts

Civil thumps Hammers

Romeo Umali

Bambo wafa atapsya ndi moto wa petrol

Romeo Umali

Malawi team shines at Huawei’s Tech4Good finals

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.