Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Mgwirizano wamaulendo apa madzi watheka

Dziko la Malawi lasayinira mgwirizano ndi kampani zomwe zimapanga komanso kuyendetsa ntchito za sitima za pamadzi kuti zidzayambitse ntchitoyi pa nyanja ya Malawi.

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, komanso nduna ya zamtengatenga, a Jacob Hara, ndi amene asayina mgwirizanowu m’malo mwa boma la Malawi.

Kampanizi zalonjeza zobwera ku Malawi posachedwa, mogwirizana ndi pempho la Dr Chakwera kuti athetse mavuto amaulendo apamadzi pa nyanja ya Malawi.

Mwambowu unachitikira munzinda wa Frankfurt m’dziko la Germany mu imodzi mwa sitima ya pamadzi zomwe amapanga m’dziko la German

Related posts

Bambo wazaka 70 akhala kundende zaka 14 chifukwa chogwililira

Alinafe Mlamba

Vuto lakuthimathima kwa magetsi Latha kunyumba yamalamulo

Mayeso Chikhadzula

Osangodalira mpira okha kumalimbikira sukulu — Chinyamula

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.