Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Development Local Local News Nkhani

Tilime mbewu zambiri zopilira ku n’gamba — Bushiri

M’neneri Shepherd Bushiri wa mema aMalawi kuti ayambe kulima mbewu zosiyanasiyana komanso zimene zili zopilira ku ng’amba ndi cholinga chofuna kupewa njala.

A Bushiri amayankhula izi ku Masasa mu mzinda wa Mzuzu komwe iwo amagawa chimanga kwa anthu amene njala idawakhudza.

“Monga ine kumunda kwanga ndinalima chinangwa chambiri ndipo chachita bwino kwambiri,” iwo anafotokoza.

A Bushiri ali ndi chikonzero chofuna kufikira maanja okwana 1 Million ndipo ati padakali pano anthu okwana pafupi-fupi 600,000 ndi amene athandizidwa kale.

Olemba: Henry Haukeya
#MBCOnlineServices

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Bus ya Bullets yachotsedwa ku khothi

Blessings Kanache

Mulhakho wa Alhomwe to elect new members on 2 March

Romeo Umali

Judiciary launches financial crimes division

Beatrice Mwape
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.