Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Mayi Monica Chakwera atsogolera amayi pa mapemphero a tsiku la a mayi

Mai wa fuko lino, Madam Monica Chakwera,  lero akutsogolera amayi m’dziko muno pa mwambo wa tsiku la mapemphero a amayi pa dziko lonse.

Mwambowu ukuchitikira pabwalo la masewero la Kamuzu mu mzinda wa Blantyre.

Pa 1 March chaka chilichonse ndi tsiku limene linapatulidwa kukhala tsiku la mapemphero a mayi pa dziko lonse.

Mutu wamapempherowa chaka chino ndi “Ndikupemphani inu kulolerana wina ndi mzake  mwachikondi” (Aefeso 4:1-8).

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

THOUSANDS ATTEND LATE MWAMBUNGU’S BURIAL

MBC Online

Big Brother Naija returns

MBC Online

Rehabilitation works on Kaombe River M5 bridges on course

Eunice Ndhlovu
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.