Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Mayi Monica Chakwera atsogolera amayi pa mapemphero a tsiku la a mayi

Mai wa fuko lino, Madam Monica Chakwera,  lero akutsogolera amayi m’dziko muno pa mwambo wa tsiku la mapemphero a amayi pa dziko lonse.

Mwambowu ukuchitikira pabwalo la masewero la Kamuzu mu mzinda wa Blantyre.

Pa 1 March chaka chilichonse ndi tsiku limene linapatulidwa kukhala tsiku la mapemphero a mayi pa dziko lonse.

Mutu wamapempherowa chaka chino ndi “Ndikupemphani inu kulolerana wina ndi mzake  mwachikondi” (Aefeso 4:1-8).

Related posts

Phungu apereka chipinda chogonamo atsikana pa sukulu ya Sharpevalle

Rabson Kondowe

Macra rolls out Campus Radio Project

Romeo Umali

Bungwe la SFFRFM lati zokonzekera AIP zili m’chimake

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.