Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Mayi Monica Chakwera atsogolera amayi pa mapemphero a tsiku la a mayi

Mai wa fuko lino, Madam Monica Chakwera,  lero akutsogolera amayi m’dziko muno pa mwambo wa tsiku la mapemphero a amayi pa dziko lonse.

Mwambowu ukuchitikira pabwalo la masewero la Kamuzu mu mzinda wa Blantyre.

Pa 1 March chaka chilichonse ndi tsiku limene linapatulidwa kukhala tsiku la mapemphero a mayi pa dziko lonse.

Mutu wamapempherowa chaka chino ndi “Ndikupemphani inu kulolerana wina ndi mzake  mwachikondi” (Aefeso 4:1-8).

Related posts

Balaka residents concerned over environmental, health risks from mining activities

Rabson Kondowe

CDH Bank bolsters Presidential Charity Golf

Romeo Umali

Mtengo wa Chocolate utha kukwera

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.