Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Kapusa aikidwa m’manda

Mwambo oika mmanda malemu Geofrey Kapusa uli mkati mmudzi mwa Mkanda kwa Ngulumia ku Zomba, komwe ndi kumudzi kwawo.

Anthu osiyanasiyana, kuphatikizapo aphungu anyumba yamalamulo, mkulu wa Malawi Broacasting Corporation a George Kasakula ndi ena ochuluka ali nawo pamwambowu.

Mwana wake oyamba wa Geofrey, Elizabeth, anati ndi okondwa kuti bambo ake amwalira ali okondwa chifukwa anali atapereka moyo wawo m’manja mwa chauta.

Iye wathokoza anthu osiyanasiyana monga nduna ya zamadzi, mayi Abida Mia komanso MBC chifukwa chothandiza bambo ake kuyambira ali ku chipatala kufikira pamene akuyikidwa m’manda.

Related posts

Councils urged to make 2025/2026 budgets realistic

Romeo Umali

Bambo mfumu alimbikitsa anthu kukhala olimbikira pa ntchito za Mulungu

Mayeso Chikhadzula

Expert touts commercial agriculture financing

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.