Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

MBC yati Kapusa anali katakwe

Mkulu wa MBC a George Kasakula ati malemu Geoffrey Kapusa anali munthu yemwe anali katakwe pantchito youlutsa mawu pa kanema komanso kuongolera tsogolo lankhani zoulutsa mawu pakanema m’dziko muno.

A Kasakula anena izi pamwambo oika m’manda a Kapusa, umene uli mkati kumudzi kwawo kwa malemwuwa.

Naye phungu wadera lakummwera kwa boma la Machinga, a Grant Ndecha, anati derali linali lokondwa kaamba kakuti linali ndi munthu yemwe achinyamata amadalira powalimbikitsa pa maphunziro kuti nawo adzakhale ndi ntchito yapamwamba.

MBC yakhala ikuthandiza a Kapusa kuyambira akudwala kufikira pano.

Related posts

MEHA LAKESHORE CONFERENCE ON

Blessings Kanache

New recruits urged to serve Malawians with honour

Blessings Kanache

Ulumali si kulephera — Papkid

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.