Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Mwambo wa chikumbutso wayamba ku Mulanje

Mneneri Shepherd Bushiri ndi mmodzi wa atsogoleri azipembedzo omwe afika ku Mulanje, komwe mwambo wachikumbutso Cha Namondwe Freddy ukuchitikira.

Bushiri wakhala akuthandiza anthu okhudzidwa ndi Namondweyu munjira zosiyanasiyana monga chakudya, ndalama mwazina.

Masabata apitawa, iye anayamikira boma pomulola kugawa chakudya komanso kutenga nawo gawo pa chitukuko cha dziko lino.

Olemba: Blessings Cheleuka
#MBCOnlineServices

Related posts

1,000 CUSTOMER WIN BIG IN TNM CHRISTMAS PROMOTION

MBC Online

Dedza DC establishes bursary committees to enhance support for students

Romeo Umali

Kalima rescues Silver Strikers

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.