Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Mwambo wa chikumbutso wayamba ku Mulanje

Mneneri Shepherd Bushiri ndi mmodzi wa atsogoleri azipembedzo omwe afika ku Mulanje, komwe mwambo wachikumbutso Cha Namondwe Freddy ukuchitikira.

Bushiri wakhala akuthandiza anthu okhudzidwa ndi Namondweyu munjira zosiyanasiyana monga chakudya, ndalama mwazina.

Masabata apitawa, iye anayamikira boma pomulola kugawa chakudya komanso kutenga nawo gawo pa chitukuko cha dziko lino.

Olemba: Blessings Cheleuka
#MBCOnlineServices

Related posts

ILO CALLS FOR ACCELERATION OF ANTI-CHILD LABOUR EFFORTS

MBC Online

ACB drills council on Corruption Risk Assessment

Rabson Kondowe

Chitipa Police rescue suspected thief from angry mob

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.